Job 20:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adzangozimirira ngati maloto, ndipo sadzapezekanso. Adzachotsedwa ngati zinthu zoonekera anthu kutulo usiku.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Adzauluka ngati loto, osapezekanso; nadzaingidwa ngati masomphenya a usiku.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Adzazimirira ngati maloto ndipo sadzapezekanso, adzachotsedwa ngati masomphenya a usiku.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adzauluka ngati loto, osapezekanso; Nadzaingidwa ngati masomphenya a usiku.