Job 21:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana ao amaseŵera pa bwalo, namavinavina ngati anaankhosa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Atulutsa makanda ao ngati gulu, ndi ana ao amavinavina.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amatulutsa ana awo ngati gulu la nkhosa; makanda awo amavinavina pabwalo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Aturutsa makanda ao ngati gulu, Ndi ana ao amabvinabvina.