Job 21:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Anthuwo amauza Mulungu kuti, ‘Tichokereni! Sitifuna kudziŵa njira zanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma adati kwa Mulungu, Tichokereni; pakuti sitifuna kudziwa njira zanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma anthuwo amawuza Mulungu kuti, ‘Tichokereni!’ Ife tilibe chikhumbokhumbo chofuna kudziwa njira zanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma adati kwa Mulungu, Ticokereni; Pakuti sitifuna kudziwa njira zanu.