Job 21:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwowo akuti amapambana chifukwa cha ntchito zao. Koma ineyo maganizo amenewo sindigwirizana nawo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, zokoma zao sizili m'dzanja lao; (koma uphungu wa oipa unditalikira.)
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Komatu ulemerero wawo suli mʼmanja mwawo, koma ine ndimakhala patali ndi uphungu wa anthu oyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, zokoma zao siziri m'dzanja lao; (Koma uphungu wa oipa unditalikira.)