Job 21:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Nkangati nyale ya oipa idazimapo? Nkangati tsoka limaŵagwera? Nkangati Mulungu amaŵakwiyira naŵalanga?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati nyali za oipa zizimidwa kawirikawiri? Ngati tsoka lao liwagwera? Ngati Mulungu awagawira zowawa mu mkwiyo wake?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma nʼkangati kamene nyale ya anthu oyipa imazimitsidwa? Nʼkangati kamene tsoka limawagwera? Nʼkangati kamene Mulungu amawakwiyira ndi kuwalanga?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati nyali za oipa zizimidwa kawiri kawiri? Ngati tsoka lao liwagwera? Ngati Mulungu awagawira zowawa mu mkwiyo wace?