Job 21:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja amati, ‘Mulungu amalanga mwana chifukwa cha machimo a bambo wake.’ Ai, koma Mulungu aŵabwezere chilango ochimwawo, kuti adziŵedi kuti Mulungu ndiye amalanga ochimwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mukuti, Mulungu asungira ana ake a munthu choipa chake, ambwezere munthuyo kuti achidziwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Paja amati, ‘Mulungu amalanga ana chifukwa cha machimo abambo awo.’ Koma Mulungu amabwezera chilango munthuyo, kuti adziwe kuti Mulungu amalangadi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mukuti, Mulungu asungira ana ace a munthu coipa cace, Ambwezere munthuyo kuti acidziwe.