Job 21:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ena amafa mtima wao uli woŵaŵa, osalaŵapo chabwino chilichonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mnzake akufa ali nao mtima wakuwawa, osalawa chokoma konse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wina amamwalira ali wowawidwa mtima, wosalawapo chinthu chabwino chilichonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mnzace akufa ali nao mtima wakuwawa, Osalawa cokoma konse.