Job 21:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ndikudziŵa zimene mukuganiza, ndikudziŵanso chiwembu chanu chimene mukuti mundichite.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, ndidziwa maganizo anu, ndi chiwembu mundilingirira moipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndikudziwa bwino zimene mukuganiza, ziwembu zanu zomwe mukuti mundichitire.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, ndidziwa maganizo anu, Ndi ciwembu mundilingirira moipa,