Job 21:30 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pa tsiku lakuti Mulungu alanga anthu, munthu woipa salangidwa konse. Amapulumuka pa tsiku loonekera mkwiyo wa Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zakuti munthu woipa asungika tsiku la tsoka? Natulutsidwa tsiku la mkwiyo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zakuti munthu woyipa amasungidwa chifukwa cha tsiku la tsoka, kuti amapulumutsidwa chifukwa cha tsiku la ukali wa Mulungu?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zakuti munthu woipa asungika tsiku la tsoka? Naturutsidwa tsiku la mkwiyo?