Job 21:34 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nanga inu mudzandisangalatsa bwanji ndi mau opanda pake? Zimene mwayankhazi ndi mabodza okhaokha.” Elifazi
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Potero munditonthozeranji nazo zopanda pake, popeza m'mayankho mwanu mutsala mabodza okha?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Nanga inu mudzanditonthoza bwanji ine ndi mawu anu opandapakewo palibe chimene chatsala kuti muyankhe koma mabodza basi!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Potero munditonthozeranji nazo zopanda pace, Popeza m'mayankho mwanu mutsala mabodza okha?