Job 21:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi ine ndimadandaulira munthu? Tsono ndilekerenji kupsa mtima?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi ine, kudandaula kwanga, ndidandaulira munthu? Ndipo ndilekerenji kupsa mtima?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi ine ndikudandaulira munthu? Tsono ndilekerenji kupsa mtima?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi ine, kudandaula kwanga, ndidandaulira munthu? Ndipo ndilekerenji kupsa mtima?