Job 21:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikaganiza zimenezo, ndimachita mantha, ndimanjenjemera kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndikangokumbukira ndivutika mtima, ndi thupi langa lichita nyaunyau.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndikamaganiza zimenezi ndimachita mantha kwambiri; thupi langa limanjenjemera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndikangokumbukila ndibvutika mtima, Ndi thupi langa licita nyau nyau.