Job 21:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi anthu oipa amakhaliranji moyo? Bwanji amafika mpaka ukalamba, ndi kusanduka amphamvu pa ulamuliro?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Oipa akhaliranji ndi moyo, nakalamba, nalemera kwakukulu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chifukwa chiyani anthu oyipa amakhalabe ndi moyo, amakalamba ndi kusanduka amphamvu?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Oipa akhaliranji ndi moyo, Nakalamba, nalemera kwakukuru?