Job 21:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amaona zidzukulu zao, ana ao amakula bwino iwo akupenya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mbeu zao zikhazikika pamodzi nao pankhope pao, ndi ana ao pamaso pao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amaona ana awo akukhazikika pamodzi nawo, zidzukulu zawo zikukula bwino iwo akuona.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mbeu zao zikhazikika pamodzi nao pankhope pao, Ndi ana ao pamaso pao,