Job 24:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Zidzatero chifukwa choti adaŵachita nkhanza akazi amasiye, akazi opanda ana sadaŵachite zabwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Alusira chumba wosabala, osamchitira wamasiye chokoma.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amachitira nkhanza mayi wosabala ndi mayi amene alibe mwana, ndipo sakomera mtima mkazi wamasiye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Alusira cumba wosabala, Osamcitira wamasiye cokoma.