Job 28:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Koma nzeru zingapezeke kuti? Luntha lingapezeke kuti?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma nzeru, idzapezeka kuti? Ndi luntha, malo ake ali kuti?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma nzeru zingapezeke kuti? Kodi kumvetsa zinthu kumakhala kuti?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma nzeru, idzapezeka kuti? Ndi luntha, malo ace ali kuti?