Job 28:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi tsono nzeru zimachokera kuti? Nkuti kumene tingapeze luntha?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma nzeru ifuma kuti? Ndi luntha, pokhala pake pali kuti?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi tsono nzeru zimachokera kuti? Kodi kumvetsa zinthu kumakhala kuti?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma nzeru ifuma kuti? Ndi luntha, pokhala pace pali kuti?