Job 28:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Iye amayang'ana mpaka ku mathero a dziko lapansi, amaona zonse zimene zili kunsi kwa thambo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti apenyerera malekezero a dziko lapansi, naona pansi pa thambo ponse;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pakuti Iye amayangʼana mpaka ku malekezero a dziko lapansi ndipo amaona zonse za kunsi kwa thambo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti apenyerera malekezero a dziko lapansi, Naona pansi pa thambo ponse;