Job 29:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthaŵi imeneyo Mphambe anali nane, ana anga ali kwete m'mbalimu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muja Wamphamvuyonse akali nane pamodzi, ndi ana anga anandizinga;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
nthawi imene Wamphamvuzonse anali nane, ndipo ana anga anali atandizungulira mʼmbalimu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Muja Wamphamvuyonse akali nane pamodzi, Ndi ana anga anandizinga;