Job 29:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene ndinkapita ku chipata cha mzinda, pamene ndinkakonzekera zokakhala nawo pabwalopo,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muja ndinatuluka kunka kuchipata kumudzi, muja ndinakonza pokhala panga kukhwalala,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Pamene ndinkapita pa chipata cha mzinda ndi kukhala pa mpando wanga pabwalo,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Muja ndinaturuka kumka kucipata kumudzi, Muja ndinakonza pokhala panga kukhwalala,