Job 30:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi mphamvu zao zikadandipinduliranji, anthu amene nyonga zao zidatha kale?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mphamvunso ya m'manja mwao ndikadapindulanji nayo? Ndiwo anthu amene unyamata wao udatha,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi mphamvu zawo ndi za phindu lanji kwa ine, pakuti mphamvu zawo zinatha kale?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mphamvunso ya m'manja mwao ndikadapindulanji nayo? Ndiwo anthu amene unyamata wao udatha,