Job 31:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
pamenepo mkazi wanga aphikire mwamuna wina chakudya, ndipo azigona naye.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
mkazi wanga aperere wina; wina namuike kumbuyo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pamenepo mkazi wanga aphikire mwamuna wina chakudya, ndipo amuna ena azigona naye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mkazi wanga aperere wina; Wina namuike kumbuyo.