Job 32:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono ataona kuti anthu atatuwo sadamuyankhe Yobe moyenera, adapsa mtima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma pakuona Elihu kuti anthu atatuwa anasowa poyankha pakamwa pao anapsa mtima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Elihu ataona kuti anthu atatuwo analibe mawu oti ayankhulenso, iye anapsa mtima.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma pakuona Elihu kuti anthu atatuwa anasowa poyankha pakamwa pao anapsa mtima.