Job 33:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pajatu Mulungu amalankhula mwa njira zosiyanasiyana, koma anthu sazindikira zimenezo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Mulungu alankhula kamodzi, kapena kawiri, koma anthu sasamalira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pajatu Mulungu amayankhula mwa njira zosiyanasiyana, ngakhale munthu sazindikira zimenezi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Mulungu alankhula kamodzi, Kapena kawiri, koma anthu sasamalira.