Job 33:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsopano ndiyamba kulankhula, ndikuuzani za mumtima mwanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani tsono, ndatsegula pakamwa panga, lilime langa lanena m'kamwa mwanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsopano ndiyamba kuyankhula; mawu anga ali pa msonga ya lilime langa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani tsono, ndatsegula pakamwa panga, Lilime langa lanena m'kamwa mwanga.