Job 33:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye adandipulumutsa kuti ndisapite ku manda, ndidzaonanso kuŵala kwa dzuŵa!’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma anandiombola ndingatsikire kumanda, ndi moyo wanga udzaona kuunika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anapulumutsa moyo wanga kuti usapite ku manda, ndipo ndidzakhala ndi moyo ndi kuonanso kuwala kwa dzuwa.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma anandiombola ndingatsikire kumanda, Ndi moyo wanga udzaona kuunika.