Job 33:30 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amapulumutsa moyo wa munthu ku malo a imfa, kuti athe kuwonanso kuŵala kwa moyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kumbweza angalowe kumanda, kuti kuunika kwa moyo kumuwalire.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kupulumutsa moyo wa munthuyo ku manda, kuti athe kuonanso kuwala kwa moyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kumbweza angalowe kumanda, Kuti kuunika kwa moyo kumuwalire.