Job 33:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati muli ndi mau, mundiyankhe. Mulankhule, chifukwa ndifuna kuti mupezeke wolungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati muli nao mau mundiyankhe. Nenani, pakuti ndifuna kukulungamitsani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati muli nʼchoti munene, ndiyankheni; yankhulani, pakuti ine ndikufuna mupezeke wolungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati muli nao mau mundiyankhe. Nenani, pakuti ndifuna kukulungamitsani.