Job 33:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Zoonadi, ndamva zimene mwalankhula, mau anu ndaŵatsata bwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zedi mwanena m'makutu mwanga, ndinamvanso mau a kunena kwanu, akuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma inu mwayankhula ine ndikumva, ndamva mawu anuwo onena kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zedi mwanena m'makutu mwanga, Ndinamvanso mau akunena kwanu, akuti,