Job 34:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Tsono mumve, inu anthu anzerunu, Mulungu sangathe kuchita choipa, Mphambe sangathe kulakwa mpang'ono pomwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake mundimvere ine, eni nzeru inu, nkutali ndi Mulungu kuchita choipa, ndi Wamphamvuyonse kuchita chosalungama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tsono mverani ine, inu anthu anzeru zomvetsa zinthu. Mulungu sangachite choyipa ndi pangʼono pomwe, Wamphamvuzonse sangathe kuchita cholakwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace mundimvere ine, eni nzeru inu, Nkutali ndi Mulungu kucita coipa, Ndi Wamphamvuyonse kucita cosalungama.