Job 34:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amambwezera munthu potsata ntchito zake, munthuyo zinthu zimamgwera malinga ndi mayendedwe ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ambwezera munthu monga mwa ntchito yake, napezetsa munthu aliyense monga mwa mayendedwe ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye amamubwezera munthu molingana ndi ntchito zake; Mulungu amabweretsa pa munthu molingana ndi zomwe amachita.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ambwezera munthu monga mwa nchito yace, Napezetsa munthu ali yense monga mwa mayendedwe ace.