Job 34:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi ndani adampatsa Mulungu udindo wolamulira dziko lapansi? Ndani adaika dziko lapansi m'manja mwake?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anamuikiza dziko lapansi ndani? Kapena anakonzeratu dziko lonse lokhalamo anthu ndani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi anapatsa Mulungu udindo wolamulira dziko lapansi ndani? Ndani anayika Mulungu kuti azilamulira dziko lonse?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anamuikiza dziko lapansi ndani? Kapena anakonzeratu dziko lonse lokhalamo anthu ndani?