Job 34:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye akadalanda moyo wake, akadamulamula kuti mpweya wake ubwerere kwa Iye mwini,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akadzikumbukira yekha mumtima mwake, akadzisonkhanitsira yekha mzimu wake ndi mpweya wake,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mulungu akanakhala ndi maganizo oti achotse mzimu wake ndi mpweya wake,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akadzikumbukila yekha mumtima mwace, Akadzisonkhanitsira yekha mzimu wace ndi mpweya wace,