Job 34:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ngati ndinu omvetsa, mumve zimenezi, mumvetsere bwino zimene ndikunenazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati tsono uli nako kuzindikira, tamvera ichi, Tcherera khutu kunena kwanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ngati ndinu omvetsa zinthu, imvani izi; mvetserani zimene ndikunena.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati tsono uli nako kuzindikira, tamvera ici, Cherera khutu kunena kwanga.