Job 34:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mulungu amadzudzula mafumu kuti, ‘Ndinu opanda pake,’ amauza akalonga kuti, ‘Ndinu oipa.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi kuyenera kunena kwa mfumu, Wopanda pake iwe, kapena kwa akalonga, Oipa inu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi si Iye amene amanena kwa mafumu kuti, ‘Ndinu opanda pake,’ ndipo amawuza anthu otchuka, ‘Ndinu oyipa,’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi kuyenera kunena kwa mfumu, Wopanda pace iwe, Kapena kwa akalonga, Oipa inu?