Job 34:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye sachita zokondera kwa akuluakulu, kapena kulemekeza olemera kupambana osauka, pakuti onsewo Mulungu adaŵalenga ndi manja ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nanga kwa Iye wosasamalira nkhope za akalonga, wosasiyanitsa pakati pa wolemera ndi wosauka? Pakuti onsewo ndiwo ntchito ya manja ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye sakondera akalonga ndipo salemekeza anthu olemera kupambana osauka, pakuti onsewa ndi ntchito ya manja ake?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nanga kwa Iye wosasamalira nkhope za akalonga, Wosasiyanitsa pakati pa wolemera ndi wosauka? Pakuti onsewo ndiwo nchito ya manja ace.