Job 34:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwowo amafa mwadzidzidzi, pakati pa usiku Mulungu amakantha anthu, iwowo nkufa, anthu amphamvu amaŵalanda moyo mosavuta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'kamphindi akufa, ngakhale pakati pa usiku, anthu agwedezeka, napita, amphamvu achotsedwa opanda dzanja lakuwachotsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo amafa mwadzidzidzi, pakati pa usiku; anthu amachita mantha ndipo amamwalira; munthu wamphamvu amachotsedwa popanda dzanja la munthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'kamphindi akufa, ngakhale pakati pa usiku, Anthu agwedezeka, napita, Amphamvu acotsedwa opanda dzanja lakuwacotsa.