Job 34:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Palibe usiku kapena mdima wandiweyani kumene anthu ochita zoipa angathe kubisalira Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Palibe mdima kapena mthunzi wa imfa, kuti ochita zopanda pake abisaleko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Palibe malo obisika kapena a mdima wandiweyani kumene anthu ochita zoyipa angabisaleko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Palibe mdima kapena mthunzi wa imfa, Kuti ocita zopanda pace abisaleko.