Job 34:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mulungu sasoŵa kuchita kumuikira munthu wina aliyense nthaŵi yoti abwere pamaso pake kudzaweruzidwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Mulungu alibe chifukwa cha kulingiriranso za munthu, kuti afike kwa Iye kudzaweruzidwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mulungu sasowa kuti apitirizebe kufufuza munthu, kuti abwere pamaso pake kudzaweruzidwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Mulungu alibe cifukwa ca kulingiriranso za munthu, Kuti afike kwa. Iye kudzaweruzidwa.