Job 34:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye amatsitsa atsogoleri, mlandu wao osaufufuza nkomwe, ndipo m'malo mwao amaikamo ena.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Aphwanya eni mphamvu osatulutsa kubwalo mlandu wao, naika ena m'malo mwao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Popanda kufufuza, Iye amawononga anthu amphamvu ndipo mʼmalo mwawo amayikamo ena.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Aphwanya eni mphamvu osaturutsa kubwalo mlandu wao, Naika ena m'malo mwao.