Job 34:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amaŵakantha chifukwa cha kuipa kwao, anthu ena onse akupenya,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Awakantha ngati oipa, poyera pamaso pa anthu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye amawalanga chifukwa cha kuyipa kwawo, pamalo pamene aliyense akuwaona;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Awakantha ngati oipa, Poyera pamaso pa anthu.