Job 34:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adaliritsa amphaŵi kuti afuule kwa Mulungu, ndipo Iyeyo adamva kufuula kwa ovutikawo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'mwemo anafikitsa kwa Iye kufuula kwa osauka; ndipo anamva Iye kufuula kwa ozunzika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anachititsa amphawi kuti kulira kwawo kufike pamaso pake, kotero Iyeyo anamva kulira kwa amphawiwo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'mwemo anafikitsa kwa Iye kupfuula kwa osauka; Ndipo anamva Iye kupfuula kwa ozunzika.