Job 34:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi Mulungu akangoti duu, ndani anganene kuti walakwa? Akabisa nkhope yake, ndani angathe kumpenyabe. Komabe ndiye amene amasamalira munthu kapena mtundu wa anthu,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye akapatsa mpumulo adzamtsutsa ndani? Akabisa nkhope yake adzampenyerera ndani? Chikachitika pa mtundu wa anthu, kapena pa munthu, nchimodzimodzi;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati Mulungu akhala chete, ndani angamunene kuti walakwa? Akabisa nkhope yake, ndani angathe kumupenyabe? Komatu ndiye amene amayangʼana za munthu komanso mtundu wa anthu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye akapatsa mpumulo adzamtsutsa ndani? Akabisa nkhope yace adzampenyerera ndani? Cikacitika pa mtundu wa anthu, kapena pa munthu, ncimodzimodzi;