Job 34:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
kuti asalamulidwe ndi anthu osadziŵa Mulungu, ndipo asakodwe m'misampha yao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti munthu wonyoza Mulungu asachite ufumu, ndi anthu asakodwe mumsampha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuti asalamuliridwe ndi anthu osapembedza, kuti asatchere anthu misampha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kuti munthu wonyoza Mulungu asacite ufumu, Ndi anthu asakodwe mumsampha,