Job 34:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi alipo amene adauza Mulungu kuti, ‘Ndalangika, sindidzachimwanso,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti pali wina kodi anati kwa Mulungu, ndasenza kulanga kwanu, ndingakhale sindinalakwa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Mwina munthu atanena kwa Mulungu kuti, ‘Ndine wolakwa koma sindidzachimwanso,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti pali wina kodi anati kwa Mulungu, Ndasenza kulanga kwanu, ndingakhale sindinalakwa?