Job 34:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakuti aYobe anena kuti, ‘Ndine wosalakwa, koma Mulungu akukana kundiweruza molungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Yobu wanena, Ine ndine wolungama, ndipo Mulungu wandichotsera choyenera ine
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Yobu akunena kuti, ‘Ndine wosalakwa, koma Mulungu akukana kundiweruza molungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Yobu wanena, Ine ndine wolungama, Ndipo Mulungu wandicotsera coyenera ine.