Job 34:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngakhale ndine wolungama, akundiyesa wabodza. Mavuto anga ndi osatha, ngakhale ndine wosachimwa.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi ndidzinamizire? Bala langa nlosapola, ngakhale sindinalakwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale ndine wolungama mtima, akundiyesa wabodza; ngakhale ndine wosachimwa, mivi yake ikundichititsa mabala osachiritsidwa.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi ndidzinamizire? Bala langa nlosapola, ngakhale sindinalakwa.