Job 34:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi pali munthu amene angafanefane ndi aYobe? Iwoŵa apambana kunyoza Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wakunga Yobu ndani, wakumwa mwano ngati madzi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi munthu wofanana ndi Yobu ndani, amene amayankhula zamwano ngati akumwa madzi?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wakunga Yobu ndani, Wakumwa mwano ngati madzi?