Job 35:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma palibe wonena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga, amene amatithandiza ngakhale pakati pa mdima wa mavuto,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma palibe anganene, Ali kuti Mulungu Mlengi wanga, wakupatsa nyimbo usiku;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga, amene amatisangalatsa nthawi ya usiku,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma palibe anganene, Ali kuti Mulungu Mlengi wanga, Wakupatsa nyimbo usiku;