Job 35:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndiye tsono, popeza kuti ukali wake sukupereka chilango, ndipo akuchita ngati sasamalako kwambiri zochita zoipa za anthu,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo tsopano popeza analibe kumzonda m'kukwiya kwake, ndi kusamalitsa cholakwa,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango, zoyipa zambiri zimene anthu amachita,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo tsopano popeza analibe kumzonda m'kukwiya kwace, Ndi kusamalitsa colakwa,